Ndathokoza
kulikonse
kumene
mwafikako,
Lekeni
tipemphere,
tiyamike
Mulungu!
Msiiidi
Vhutsa,
ndathokoza
pokusankha
Ndathokoza
posankha
ine,
munthu
chabe
pa
dziko
lonse
Mulungu
atamandidwe,
Traineesii
Mwinga
Ndiwe
mtendere
wanga,
ndiwo
mgwirizano
umene
ndinapempha
Umo ndi moyo wa wosauka, madzi akuti lowa
Ife
awiri
Mulungu
atupala
Amen,
amen,
Vhusa
ndi
Traineesii,
muli
m'chikondi
Mulungu
adalitse
nyumba
Ukwati
wa
chaka,
ndathokoza!