[male vocals] Inu
Mulungu,
tikuyamikani;
Tibvomereza
ndinu
Ambuyathu;
Ponse,
Atate,
akugwadirani,
Ndinu
wamuyaya!
Nanu
akukuzani
amithenga,
Nanu
zam’
mwamba
ndi
zamphamvu
zake,
Nanu
angelo
a
mitundu
yonse
Akuimbirani! “
Mbuye
Woyera!
E,
Woyera
nokha!
Mbuye
Woyera!
Mbuye
wa
makamu!
Ponse
ulemu
wanu
ndi
wodzaza
Pansi
ndi
Kumwamba.”
Nanu
Atumwi
akumveka
aja,
Ndi
Aneneri
oyanjana
omwe,
Ndi
aunyinji
anakuferani
Akuyamikani.
Mpingo
woyera
wa
kwa
anthu
onse
Ukumverani,
Mfumu
ndi
Atate,
Mwana
woona
wa
ulemu
wonse,
Mzimu
Nkhoswe
yemwe.
Inu
Mulungu,
tikuyamikani;
Tibvomereza
ndinu
Ambuyathu;
Ponse,
Atate,
akugwadirani,
Ndinu
wamuyaya!
Nanu
akukuzani
amithenga,
Nanu
zam’
mwamba
ndi
zamphamvu
zake,
Nanu
angelo
a
mitundu
yonse
Akuimbirani!
Kristu
Mfumuyo
yauleme
rero!
Mwana
wosatha
wa
Atate
ndinu!
Simunanyoza
mimba
ya
namwali
Potipulumutsa.
Imfa
mutagonjetsa
ndi
zowawa,
Njira
munatsegula
tikalowe
Momwe
mukhala
Inu
ndi
Atate
Mwaulemerero.
Kumva
milandu
yathu
mudzabwera
Mutithandize,
atumiki
anu;
Mwatiwombola
nawo
mwazi
wanu:
Mutipulumutse
Mtiwerengere
mMwamba
ndi
oyera;
Mutidalitse,
ndife
anthu
anu;
Moyo
wosatha
mutipatse
tonse,
Mutilamulire.
Tsiku
ndi
tsiku
timalemekeza;
Nanu
tikukuzani
osaleka;
Mbuye,
mtisunge
tingachimwe
lero:
Mtichitire
nsisi.
Mbuye,
chifundo
chanu
chitigwere
Monga
tikhulupira
Inu
nokha;
Ndakhulupira
zedi
mwanu,
Mbuye,
Ndisagome
konse!
Nditamatu
Ambuyangayu,
Ponsepo
pali
Mlungu,
Poyenda
ife
m'njira
Poima
pali
Mlungu;
Kokwera
maganizo,
Komweko
kuli
Mlungu,
Kumwamba
ndi
pansipo
Ponsepo
pali
Mlungu.
Mulungu
ali
paja;
N'kalowa
imfa
ine
Alipo
Mlungu
wanga. (
Ali
nane,
aIi
nane,
ali
nane,
ali
nane,
Aa!
Mulungu
ali
nane!)
Ndi
maso
Ambuyathu
Apenyetsetsa
ife;
Amadalits
onse
Okhulupirira
Iye;
Amamva
timbalame,
Namveka
dziko
lonse;
Sataya
tizilombo,
Asunga
zina
zonse.
Okwawa
pansi
inu,
Oyenda
m'maddzi
inu;
Oyesa
dziko
nkwanu,
Am'mlengalenga
inu,
Nonsenu
ntchito
zake
Muona
tsiku
n'tsiku,
Saleka
kusamala
Ndi
kudalitsa
inu.
Nditama
mphamvu
yake
Ya
Mlungu
yondizinga;
N'kafoka
an'limbitsa,
N'kadwala
andichiza.
Pakundisiya
bwenzi
Mulungu
ali
paja;
N'kalowa
imfa
ine
Alipo
Mlungu
wanga.
Tiimbe
nyimbo
zotamanda
Mulungu
wathu
wabwino,
Pakuti
akondana
nawo
Anthu
okhala
padziko;
Tero
natuma
Mwana
wake,
Wakukondedwa
kalelo,
Kutiphunzitsa
ife
tonse
Za
chikondano
chakecho.
Mulungu
ndiye
wachifundo,
Nadzalandira
onsewa
Akuulula
mphulupulu
Ndi
kukondana
ndi
Yesu,
Tilondelonde
njira
yake,
Yopapatiza
yaing'ono;
Adzatilondolera
ndiye
Kutifikitsa
m'Mwambamo.
Pakuwoloka
mtsinje
wa
imfa
Dzanja
Mbuyathu
agwira;
Tikadagwira
ntchito
zake
Atipatsatu
korona;
Komwe
kulibe
masauko,
Pena
misozi
maliro;
Mulungu
tidzamtamandira,
Inde
kosalekezanso.