Mulungu wanga, iwe ndiwe moyo wanga
Eish, tikuimba lero
Ndikuyenda m'njira zanga ndili ndekha
Koma ndikumva chikhulupiliro m'mtima mwanga
Mulungu wanga, iwe ndiwe woyera
Nthawi zonse umanditsogolera m'njira zolondola
Ndikuyang'ana mmwamba, ndikuona kuwala
Dziko likuyenda, koma iwe sunasiye
Mulungu wanga ni Yesu oyera
Nigwireni zanja langa, mulungu wanga
Mulungu wanga ni Yesu oyera
Nigwireni zanja langa, mulungu wanga
Sharp sharp, tipitilire patsogolo
Nthawi zina ndikumva ngati ndatopa
Koma mawu ako amandipatsa mphamvu
Ndiwe chiyembekezo changa m'mdima
Iwe ndiwe gwero la mtendere chiuta ngwalusungu chiuta ngwalusungu oooooo ps g.o.m.a dada chinjani mutima wane napambuka namwana wanu