Frobits
🎵 A song made on Frobits

We Are Redeemed

0:000:00
Download
Make your own song
Lyrics

We

are

redeemed,

glory

to

the

Lamb!

Yes

Lord,

we

stand

in

Your

light

today.

Ndipereka

zanga

zonse

Mwaufulu

kwa

Yesu;

Ndidzamkonda

kopambana,

Tsiku

lili

lonsetu.

Ndiperekatu

Zonse

kwa

Yesu;

Ndipereka

zonse

kwa

'Nu,

Dalitseni. 2

Ndipereka

zanga

zonse

Pamapazi

a

Yesu;

Zapadziko

ndazikana,

Nditengeni

Yesu

'Nu.

Ndiperekatu

Zonse

kwa

Yesu;

Ndipereka

zonse

kwa

'Nu,

Dalitseni.

Ndipereka

zanga

zonse,

Ndipo

n'khale

wanutu;

Mzimu

wanu

'ndidziwitse

Kuti

ndine

wanudi.

Ndipereka

zanga

zonse,

Ndili

wanu

ndense

'ne;

Nditamanda

Dzina

lanu,

Aleluya,

Ambuye.

Ndiperekatu

Zonse

kwa

Yesu;

Ndipereka

zonse

kwa

'Nu,

Dalitseni.

Kwathu

sipadziko,

ndingopitirira,

Ndadzikundikira

chuma

Kumwambako;

Mngelo

akodola

pakhomo

la

m'mwamba;

Ndipo

dziko

lapansi

sindyesa

kwathu.

Mbuye

ndinu

bwenzi

langa

ndithu,

Ndichitenji

ngati

Kumwamba

sikwathu?

Mngelo

akodola

pakhomo

la

m'Mwamba,

Ndipo

dziko

lapansi

sindiyesa

kwathu.

Andiyembekeza,

chinthuchi

ndidziwa,

Mpulumutsi

wanga

wandikhulukira;

Adzandipyoletsa

pamene

ndafoka;

Ndipo

dziko

lapansi

sindiyesa

kwathu.

Mayi

watsogola

ku

Ulemerero,

Ndifuna

kugwira

dzanja

lake

konko,

Andidikiranso

pakhomo

la'Mwamba;

Ndipo

dziko

lapansi

sindiyesa

kwathu.

Mu

ulemerero

tidzakhala

m'yaya,

Oyera

mtimawo

ali

kulamira;

Ati, "

Aleluya

kwa

Mlungu

Wamphamvu."

Ndipo

dziko

lapansi

sindiyesa

kwathu.

Ambiri

tikondwera

mwa

Yesu,

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Tapeza

chipulumutso

ndithu;

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Masiku

onse

timakondwera

Pakumva

Mawu

ake

a

Yesu;

Wolalikira

tidzamumvera;

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Ife

tiyembekezera

Yesu,

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Chimwemwecho

chili

mumtimamu;

Nanga

inu?

Masiku

onse

timakondwera

Pakumva

Mawu

ake

a

Yesu;

Wolalikira

tidzamumvera;

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Titasokera

tinabwerera,

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Tadziwa

kuti

ndiwo

uchimo;

Nanga

inu?

Masiku

onse

timakondwera

Pakumva

Mawu

ake

a

Yesu;

Wolalikira

tidzamumvera;

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Tinachoka

munjira

ya

imfa,

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Takopeka

ndi

Mawu

a

Yesu;

Nanga

inu?

Masiku

onse

timakondwera

Pakumva

Mawu

ake

a

Yesu;

Wolalikira

tidzamumvera;

Nanga

inu?

Nanga

inu?

Kuli

dziko

labwino

m'Mwamba

Lakuwala

koposa

dzuwa;

Yesu

atikonzera

malo

Pokhalira

ife

komweko.

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija,

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija.

Tidzimba

komweko

nyimbo

Za

abwino

omvera

Yesu,

Sitidzamva

chisoni

ife,

Tidzakondwa

masiku

onse.

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija,

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija

Tidzatama

Atate

wathu

Kuti

Iye

'napatsa

Yesu

Kuchotsera

zochimwa

zonse,

Ndi

kutidalitsira

ife.

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija,

Bwinoli

tipita,

Tikumana

mwa

Dziko

lija

Ndine

Mbusayo

wabwino,

Ndinafera

nkhosazo;

Yotayika

ndaifuna,

Mpaka

ndataya

moyo.

Mbulu

wanding'amba

m'nthiti,

Wanding'ambanso

m'manja,

Wanding'ambira

zobvala,

Ndatsala

waumphamwi.

Nkhosa

zanga

zimandimva

Ndikaziitanazo;

Ndimazipatsa

moyowo,

Atate

nazisunga.

Mbulu

wanding'amba

m'nthiti,

Wanding'ambanso

m'manja,

Wanding'ambira

zobvala,

Ndatsala

waumphamwi.

M'kati

ali

fisiyo;

Musanyengedwa

anthuni,

Ine

ndine

Mbusayo.

Mbulu

wanding'amba

m'nthiti,

Wanding'ambanso

m'manja,

Wanding'ambira

zobvala,

Ndatsala

waumphamwi.

More songs by israel Listen to songs created by others
FROBITS